Yohane 6:47 - Buku Lopatulika47 Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Iye wokhulupirira ali nao moyo wosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Iye wokhulupirira ali nao moyo wosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 “Ndithu ndikunenetsa kuti wokhulupirira Ine, ali nawo moyo wosatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti Iye amene akhulupirira ali nawo moyo wosatha. Onani mutuwo |