Yohane 6:46 - Buku Lopatulika46 Sikuti munthu wina waona Atate, koma Iye amene ali wochokera kwa Mulungu, ameneyo waona Atate. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201446 Sikuti munthu wina waona Atate, koma Iye amene ali wochokera kwa Mulungu, ameneyo waona Atate. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa46 Sindiye kutitu wina aliyense adaona Atate ai, koma Ine ndekha amene ndidachokera kwa Mulungu; Ineyo ndi amene ndidaona Atate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero46 Palibe amene anaona Atate koma yekhayo amene achokera kwa Mulungu; yekhayo ndiye anaona Atate. Onani mutuwo |