Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 6:48 - Buku Lopatulika

48 Ine ndine mkate wamoyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Ine ndine mkate wamoyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Ine ndine chakudya chopatsa moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Ine ndine chakudya chamoyo.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:48
6 Mawu Ofanana  

Odala ali akumva njala ndi ludzu la chilungamo; chifukwa adzakhuta.


Chifukwa chake Ayuda anang'ung'udza za Iye, chifukwa anati, Ine ndine mkate wotsika Kumwamba.


Mkate wamoyo wotsika Kumwamba Ndine amene. Ngati munthu wina akadyako mkate umene, adzakhala ndi moyo kosatha. Inde, ndipo mkate umene ndidzapatsa Ine, ndiwo thupi langa, ukhale moyo wa dziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa