Yohane 6:30 - Buku Lopatulika30 Chifukwa chake anati kwa Iye, Ndipo muchita chizindikiro chanji, kuti tione ndi kukhulupirira Inu? Muchita chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Chifukwa chake anati kwa Iye, Ndipo muchita chizindikiro chanji, kuti tione ndi kukhulupirira Inu? Muchita chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Iwo adafunsanso kuti, “Mungatiwonetse chizindikiro chotani kuti tikachiwona tikukhulupirireni? Nanga muchitapo chiyani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Choncho iwo anamufunsa Iye kuti, “Kodi mudzatipatsa chizindikiro chodabwitsa chotani kuti ife tichione ndi kukhulupirira Inu? Kodi mudzachita chiyani? Onani mutuwo |