Yohane 6:31 - Buku Lopatulika31 Atate athu anadya mana m'chipululu; monga kwalembedwa, Mkate wochokera m'mwamba anawapatsa iwo kudya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Atate athu anadya mana m'chipululu; monga kwalembedwa, Mkate wochokera m'mwamba anawapatsa iwo kudya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Makolo athu ankadya mana m'chipululu muja, monga Malembo akunenera kuti, ‘Ankaŵapatsa chakudya chochokera Kumwamba kuti adye.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Makolo athu akale anadya mana mʼchipululu; monga zalembedwa: ‘anawapatsa buledi wochokera kumwamba kuti adye.’ ” Onani mutuwo |