Yohane 6:29 - Buku Lopatulika29 Yesu anayankha nati kwa iwo, Ntchito ya Mulungu ndi iyi, kuti mukhulupirire Iye amene Iyeyo anamtuma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Yesu anayankha nati kwa iwo, Ntchito ya Mulungu ndi iyi, kuti mukhulupirire Iye amene Iyeyo anamtuma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adaŵayankha kuti, “Chimene Mulungu afuna kuti muchite nchakuti mundikhulupirire Ineyo amene Mulungu adandituma.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Yesu anayankha kuti, “Ntchito ya Mulungu ndi iyi: Kukhulupirira Iye amene anamutuma.” Onani mutuwo |