Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:16 - Buku Lopatulika

16 Koma pofika madzulo, ophunzira ake anatsikira kunyanja;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma pofika madzulo, ophunzira ake anatsikira kunyanja;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 M'mene kunkayamba kuda, ophunzira ake a Yesu adatsikira ku nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Pofika madzulo, ophunzira ake anatsikira ku nyanja,

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:16
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pofika madzulo ngalawa inali pakati pa nyanja, ndi Iye yekha pamtunda.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


ndipo pamene adalowa m'ngalawa, analikuoloka nyanja kunka ku Kapernao. Ndipo kutada pamenepo, koma Yesu asanadze kwa iwo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa