Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 6:13 - Buku Lopatulika

13 Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Adatoladi zotsala zonse za buledi msanu uja, nadzaza madengu khumi ndi aŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Choncho iwo anasonkhanitsa makombo nadzaza madengu khumi ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 6:13
9 Mawu Ofanana  

Potero anawagawira, nadya, nasiyapo, monga mwa mau a Yehova.


Ndipo Amaziya anati kwa munthu wa Mulungu, Koma nanga titani nao matalente zana limodzi ndinapatsa ankhondo a Israele? Nati munthu wa Mulungu, Yehova ali nazo zoposa izi kukupatsani.


Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri.


Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zikwanira bwanji ambiri otere?


Koma Mulungu wanga adzakwaniritsa chosowa chanu chilichonse monga mwa chuma chake mu ulemerero mwa Khristu Yesu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa