Yohane 6:13 - Buku Lopatulika13 Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pomwepo anasonkhanitsa, nadzaza madengu khumi ndi awiri ndi makombo a mikate isanuyo yabarele, amene anatsalira anadyawo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Adatoladi zotsala zonse za buledi msanu uja, nadzaza madengu khumi ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho iwo anasonkhanitsa makombo nadzaza madengu khumi ndi awiri. Onani mutuwo |