Yohane 6:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo pamene adakhuta, Iye ananena kwa ophunzira ake, Sonkhanitsani makombo kuti kasatayike kanthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo pamene adakhuta, Iye ananena kwa ophunzira ake, Sonkhanitsani makombo kuti kasatayike kanthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu onsewo atakhuta, Yesu adauza ophunzira ake kuti, “Tolani zotsala kuti pasatayikepo kanthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo atakhuta, Iye anati kwa ophunzira ake, “Tolani zotsala kuti pasawonongeke kanthu.” Onani mutuwo |