Yohane 5:8 - Buku Lopatulika8 Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yesu ananena naye, Tauka, yalula mphasa yako, nuyende. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Yesu adamlamula kuti, “Dzuka, tenga mphasa yako, yamba kuyenda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo Yesu anati kwa iye, “Imirira! Nyamula mphasa yako yamba kuyenda.” Onani mutuwo |