Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:7 - Buku Lopatulika

7 Wodwalayo anayankha, Ambuye, ndilibe wondiviika ine m'thamanda, paliponse madzi avundulidwa; koma m'mene ndilinkudza ine, wina atsika ndisanatsike ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Wodwalayo anayankha, Ambuye, ndilibe wondiviika ine m'thamanda, paliponse madzi avundulidwa; koma m'mene ndilinkudza ine, wina atsika ndisanatsike ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Wodwalayo adati, “Ambuye, ndilibe munthu wondiloŵetsa m'dziŵemu madzi akavundulidwa. Ndikati ndiloŵemo, wina waloŵa kale.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Wodwalayo anayankha kuti, “Ambuye, ndilibe wina aliyense woti angandithandize kulowa mʼdziwe pamene madzi avundulidwa. Pamene ndikuyesera kuti ndilowemo, wina amalowamo ine ndisanalowemo.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:7
10 Mawu Ofanana  

Penyani kudzanja lamanja ndipo muone; palibe wondidziwa; pothawirapo pandisowa; palibe mmodzi wosamalira moyo wanga.


Pakuti adzapulumutsa waumphawi wofuulayo; ndi wozunzika amene alibe mthandizi.


Koma pali thamanda mu Yerusalemu pa Chipata cha Nkhosa, lotchedwa mu Chihebri Betesida, lili ndi makonde asanu.


M'menemo munagona khamu lalikulu la anthu odwala, akhungu, opunduka miyendo, opuwala.


Yesu, pakuona ameneyo alikugona, ndipo anadziwa kuti anatero nthawi yaikulu pamenepo, ananena naye, Ufuna kuchiritsidwa kodi?


Pakuti pamene tinali chikhalire ofooka, pa nyengo yake Khristu anawafera osapembedza.


Kodi simudziwa kuti iwo akuchita makani a liwiro, athamangadi onse, koma mmodzi alandira mfupo? Motero thamangani, kuti mukalandire.


Popeza Yehova adzaweruza anthu ake, nadzachitira nsoni anthu ake; pakuona Iye kuti mphamvu yao yatha, wosatsala womangika kapena waufulu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa