Yohane 5:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo pomwepo munthuyu anachira, nayalula mphasa yake, nayenda. Koma tsiku lomwelo linali la Sabata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pompo munthuyo adachiradi, nanyamula mphasa yake nkuyamba kuyenda. Tsikulo linali la Sabata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nthawi yomweyo munthuyo anachiritsidwa. Iye ananyamula mphasa yake nayamba kuyenda. Tsiku limene izi zinachitika linali la Sabata. Onani mutuwo |