Yohane 5:10 - Buku Lopatulika10 Chifukwa chake Ayuda ananena kwa wochiritsidwayo, Ndi Sabata, ndipo sikuloledwa kwa iwe kuyalula mphasa yako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chifukwa chake Ayuda ananena kwa wochiritsidwayo, Ndi Sabata, ndipo sikuloledwa kwa iwe kuyalula mphasa yako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Choncho Ayuda adauza munthu amene adachirayo kuti, “Lero mpa Sabata. Malamulo athu sakulola kunyamula mphasa yako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo Ayuda anati kwa munthu amene anachiritsidwayo, “Lero ndi la Sabata; lamulo silikulola iwe kunyamula mphasa yako.” Onani mutuwo |