Yohane 5:39 - Buku Lopatulika39 Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Mumaphunzira Malembo mozama, chifukwa mumaganiza kuti mupezamo moyo wosatha. Ndipotu ndi Malembo omwewo amene akundichitira umboni! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Inu mumasanthula malemba chifukwa mumaganiza kuti mʼmalembamo muli moyo wosatha. Awa ndi malemba amene akundichitira umboni. Onani mutuwo |