Yohane 5:40 - Buku Lopatulika40 ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 ndipo simufuna kudza kwa Ine, kuti mukhale nao moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Komabe inu simufuna kudza kwa Ine kuti mukhale ndi moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Koma inu mukukana kubwera kwa Ine kuti mukhale ndi moyo. Onani mutuwo |
Chifukwa chanji ndinafika osapeza munthu? Ndi kuitana koma panalibe wina woyankha? Kodi dzanja langa lafupika konse, kuti silingathe kuombola? Pena Ine kodi ndilibe mphamvu zakupulumutsa? Taona pa kudzudzula kwanga ndiumitsa nyanja, ndi kusandutsa mitsinje chipululu; nsomba zake zinunkha chifukwa mulibe madzi, ndipo zifa ndi ludzu.