Yohane 5:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo mulibe mau ake okhala mwa inu; chifukwa kuti amene Iyeyu anatuma, inu simumkhulupirira ameneyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo mulibe mau ake okhala mwa inu; chifukwa kuti amene Iyeyu anatuma, inu simumkhulupirira ameneyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Mau ao sakhala mwa inu, chifukwa simumkhulupirira amene Atatewo adamtuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 kapena mawu ake kukhala mwa inu, pakuti simukhulupirira Iye amene anamutuma. Onani mutuwo |