Yohane 5:32 - Buku Lopatulika32 Wochita umboni wa Ine ndi wina; ndipo ndidziwa kuti umboni umene Iye andichitire Ine uli woona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Wochita umboni wa Ine ndi wina; ndipo ndidziwa kuti umboni umene Iye andichitire Ine uli woona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Pali wina wondichitira umboni, ndipo ndikudziŵa kuti umboni umene iye amandichitirawo ngwoona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Alipo wina amene amandichitira umboni wabwino. Ine ndikudziwa kuti umboni wake wonena za Ine ndi woona. Onani mutuwo |