Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:31 - Buku Lopatulika

31 Ngati ndichita umboni wa Ine ndekha, umboni wanga suli woona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ngati ndichita umboni wa Ine ndekha, umboni wanga suli woona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 “Ngati ndidzichitira ndekha umboni, umboni wangawo ngwosakwanira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 “Ngati ndidzichitira umboni ndekha, umboni wanga si woona.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:31
4 Mawu Ofanana  

Wina akutume, si m'kamwa mwako ai; mlendo, si milomo ya iwe wekha.


Yesu anayankha, Ngati Ine ndidzilemekeza ndekha, ulemerero wanga uli chabe; Atate wanga ndiye wondilemekeza Ine; amene munena za Iye, kuti ndiye Mulungu wanu;


Ndipo kwa mngelo wa Mpingo wa ku Laodikea lemba: Izi anena Ameni'yo, mboni yokhulupirika ndi yoona, woyamba wa chilengo cha Mulungu:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa