Yohane 5:27 - Buku Lopatulika27 ndipo anampatsa Iye mphamvu ya kuchita mlandu, pakuti ali Mwana wa Munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 ndipo anampatsa Iye mphamvu ya kuchita mlandu, pakuti ali Mwana wa Munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ndipo adapatsa Mwanayo mphamvu ya kuweruza anthu, chifukwa ndi Mwana wa Munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Ndipo wamupatsa Iye ulamuliro woweruza chifukwa ndi Mwana wa Munthu. Onani mutuwo |