Yohane 5:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti Atate saweruza munthu aliyense, koma anapereka kuweruza konse kwa Mwana; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti Atate saweruza munthu aliyense, koma anapereka kuweruza konse kwa Mwana; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Atate saweruza munthu aliyense, koma adaika Mwana wake kuti akhale woweruza pa zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Komanso, Atate saweruza aliyense koma wapereka kwa Mwana ulamuliro woweruzawo, Onani mutuwo |