Yohane 5:23 - Buku Lopatulika23 kuti onse akalemekeze Mwana, monga alemekeza Atate. Wosalemekeza Mwana salemekeza Atate amene anamtuma Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 kuti onse akalemekeze Mwana, monga alemekeza Atate. Wosalemekeza Mwana salemekeza Atate amene anamtuma Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Atate amafuna kuti anthu onse azilemekeza Mwana, monga momwe amalemekezera Atate. Munthu amene salemekeza Mwana, salemekezanso Atate amene adamtuma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 kuti aliyense alemekeze Mwanayo monga momwe amalemekezera Atate. Munthu amene salemekeza Mwana salemekezanso Atate amene anamutuma Mwanayo. Onani mutuwo |