Yohane 5:21 - Buku Lopatulika21 Pakuti monga Atate aukitsa akufa, nawapatsa moyo, momwemonso Mwana apatsa moyo iwo amene Iye afuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Pakuti monga Atate aukitsa akufa, nawapatsa moyo, momwemonso Mwana apatsa moyo iwo amene Iye afuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Monga Atate amaukitsa akufa, naŵapatsa moyo, moteronso Mwana amapatsa moyo kwa amene Iye afuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Pakuti monga Atate amaukitsa akufa nawapatsa moyo, momwemonso Mwana amapereka moyo kwa amene Iye akufuna. Onani mutuwo |