Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo chifukwa cha ichi Ayuda analondalonda Yesu, popeza anachita izo tsiku la Sabata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo chifukwa cha ichi Ayuda analondalonda Yesu, popeza anachita izo tsiku la Sabata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Popeza kuti linali tsiku la Sabata pamene Yesu adaachita zimenezi, Ayuda adayamba kumuvutitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ndipo popeza Yesu amachita zinthu izi tsiku la Sabata, Ayuda anayamba kumulondalonda.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:16
15 Mawu Ofanana  

Pomwepo ananena Iye kwa munthuyo, Tansa dzanja lako. Ndipo iye analitansa, ndipo linabwezedwa lamoyo longa linzake.


Ndipo Afarisi anatuluka, ndipo pomwepo anamkhalira upo ndi Aherode, wakumuononga Iye.


Koma iwowo anagwidwa misala; nalankhulana wina ndi mnzake kuti amchitire Yesu chiyani.


Ndipo umene ndiwo umboni wa Yohane, pamene Ayuda anatuma kwa iye ansembe ndi Alevi a ku Yerusalemu akamfunse iye, Ndiwe yani?


Anafunanso kumgwira Iye; ndipo anapulumuka m'dzanja lao.


Kumbukirani mau amene Ine ndinanena kwa inu, Kapolo sali wamkulu ndi mbuye wake. Ngati anandilondalonda Ine, adzakulondalondani inunso; ngati anasunga mau anga, adzasunga anunso.


Chifukwa chake Ayuda ananena kwa wochiritsidwayo, Ndi Sabata, ndipo sikuloledwa kwa iwe kuyalula mphasa yako.


Koma wochiritsidwayo sanadziwe kuti anali ndani; pakuti Yesu anachoka kachetechete, popeza panali anthu aunyinji m'malo muja.


Munthuyo anachoka, nauza Ayuda, kuti ndiye Yesu amene adamchiritsa.


Koma Yesu anayankha iwo, Atate wanga amagwira ntchito kufikira tsopano, Inenso ndigwira ntchito.


Chifukwa cha ichi Ayuda anaonjeza kufuna kumupha, si chifukwa cha kuswa tsiku la Sabata kokha, komatu amatchanso Mulungu Atate wake wa Iye yekha; nadziyesera wolingana ndi Mulungu.


Yesu anayankha nati kwa iwo, Ndinachita ntchito imodzi, ndipo muzizwa monse.


Pamenepo ena a iwo a ku Yerusalemu ananena, Kodi suyu amene afuna kumupha?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa