Yohane 5:17 - Buku Lopatulika17 Koma Yesu anayankha iwo, Atate wanga amagwira ntchito kufikira tsopano, Inenso ndigwira ntchito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Koma Yesu anayankha iwo, Atate wanga amagwira ntchito kufikira tsopano, Inenso ndigwira ntchito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma Yesu adaŵauza kuti, “Atate anga akugwira ntchito mpaka tsopano, nanenso ndikugwira ntchito.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Yesu anawawuza kuti, “Atate anga amagwira ntchito nthawi zonse mpaka lero lino, ndipo Inenso ndili pa ntchito.” Onani mutuwo |