Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 5:13 - Buku Lopatulika

13 Koma wochiritsidwayo sanadziwe kuti anali ndani; pakuti Yesu anachoka kachetechete, popeza panali anthu aunyinji m'malo muja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Koma wochiritsidwayo sanadziwe kuti anali ndani; pakuti Yesu anachoka kachetechete, popeza panali anthu aunyinji m'malo muja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Koma wochirayo sadamdziŵe, popeza kuti Yesu anali ataloŵerera m'kati mwa anthu ambiri amene anali pamenepo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Munthu amene anachiritsidwayo sanadziwe kuti anali ndani, pakuti Yesu anangolowera mʼgulu la anthu ndi kupita.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 5:13
6 Mawu Ofanana  

Ndipo maso ao anatseguka, ndipo anamzindikira Iye; ndipo anawakanganukira Iye, nawachokera.


Koma Iye anapyola pakati pao, nachokapo.


Yesu ananena naye, Kodi ndili ndi inu nthawi yaikulu yotere, ndipo sunandizindikire, Filipo? Iye amene wandiona Ine waona Atate; unena iwe bwanji, Mutionetsere Atate?


Anamfunsa, Munthuyo ndani wonena ndi iwe, Yalula mphasa yako, nuyende?


Zitapita izi Yesu anampeza mu Kachisi, nati kwa iye, Taona, wachiritsidwa; usachimwenso, kuti chingakugwere choipa choposa.


Pamenepo anatola miyala kuti amponye Iye; koma Yesu anabisala, natuluka mu Kachisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa