Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:49 - Buku Lopatulika

49 Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

49 Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

49 Ndunayo idati, “Ndapota nanu Ambuye, tiyeni mwana wanga asanafe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:49
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ine ndine wozunzika ndi waumphawi; koma Ambuye andikumbukira ine. Inu ndinu mthandizi wanga, ndi Mpulumutsi wanga, musamachedwa, Mulungu wanga.


nanena, kuti, Kamwana kanga kabuthu kalinkutsirizika; ndikupemphani Inu mufikeko, muike manja anu pa iko, kuti kapulumuke, ndi kukhala ndi moyo.


Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira.


Yesu ananena naye, Muka, mwana wako ali ndi moyo. Munthuyo anakhulupirira mau amene Yesu anatero naye, namuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa