Yohane 4:49 - Buku Lopatulika49 Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Mkuluyo ananena kwa Iye, Ambuye, tsikani asanafe mwana wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Ndunayo idati, “Ndapota nanu Ambuye, tiyeni mwana wanga asanafe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Nduna ya mfumuyo inati, “Ambuye tiyeni mwana wanga asanafe.” Onani mutuwo |