Yohane 4:48 - Buku Lopatulika48 Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Pamenepo Yesu anati kwa iye, Ngati simuona zizindikiro ndi zozizwa, simudzakhulupirira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Yesu adamuuza kuti, “Mukapanda kuwona zizindikiro ndi zozizwitsa, simukhulupirira ai.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Yesu anawawuza iwo kuti, “Anthu inu pokhapokha mutaona zizindikiro zodabwitsa, simudzakhulupirira.” Onani mutuwo |