Yohane 4:50 - Buku Lopatulika50 Yesu ananena naye, Muka, mwana wako ali ndi moyo. Munthuyo anakhulupirira mau amene Yesu anatero naye, namuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 Yesu ananena naye, Muka, mwana wako ali ndi moyo. Munthuyo anakhulupirira mau amene Yesu anatero naye, namuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Yesu adamuuza kuti, “Pitani! Mwana wanu wachira.” Munthuyo adakhulupiriradi mau a Yesuwo, ndipo adapita kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Yesu anayankha kuti, “Pita. Mwana wako adzakhala ndi moyo.” Munthuyo anakhulupirira mawu a Yesu ndipo ananyamuka. Onani mutuwo |