Yohane 4:45 - Buku Lopatulika45 Chifukwa chake pamene anadza ku Galileya, Agalileya anamlandira Iye, atakaona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pachikondwerero; pakuti iwonso ananka kuchikondwerero. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Chifukwa chake pamene anadza ku Galileya, Agalileya anamlandira Iye, atakaona zonse zimene anazichita m'Yerusalemu pachikondwerero; pakuti iwonso ananka kuchikondwerero. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Komabe pamene adafika ku Galileya, Agalileya adamlandira popeza kuti eniakewo nawonso adaapita ku Yerusalemu ku chikondwerero cha Paska, ndipo adaaona zonse zimene Yesu adaachita pachikondwereropo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Iye atafika ku Galileya, Agalileya anamulandira. Iwo anali ataona zonse zimene anazichita mu Yerusalemu pa phwando la Paska, pakuti iwonso anali komweko. Onani mutuwo |