Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:44 - Buku Lopatulika

44 Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Mwiniwakeyo anali atanena kuti, “Mneneri, anthu akwao samchitira ulemu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 (Tsopano Yesu mwini ananena kale kuti mneneri salandira ulemu mʼdziko lake).

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:44
3 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Ndipo Yesu ananena kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu, koma m'dziko la kwao ndimo, ndi pakati pa abale ake, ndi m'nyumba yake.


Ndipo Iye anati, Indetu, ndinena kwa inu, kuti, Palibe mneneri alandirika kudziko la kwao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa