Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:43 - Buku Lopatulika

43 Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Atapita masiku aŵiriwo, Yesu adachoka napita ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:43
8 Mawu Ofanana  

ndipo anachoka ku Nazarete nadza nakhalitsa Iye mu Kapernao wa pambali pa nyanja, m'malire a Zebuloni ndi Nafutali:


Anadza naye kwa Yesu. M'mene anamyang'ana iye, anati, Uli Simoni mwana wa Yohane; udzatchedwa Kefa (ndiko kusandulika Petro).


Chifukwa chake pamene Asamariya anadza kwa Iye, anamfunsa akhale nao; ndipo anakhala komweko masiku awiri.


Pakuti Yesu mwini anachita umboni kuti, Mneneri alibe ulemu m'dziko la kwao.


Chifukwa chake Yesu anadzanso ku Kana wa mu Galileya, kumene anasandutsa madzi vinyo. Ndipo kunali mkulu wina wa mfumu, mwana wake anadwala mu Kapernao.


Ndipo ndinena kuti Khristu anakhala mtumiki wa mdulidwe, chifukwa cha choonadi cha Mulungu, kuti alimbikitse malonjezo opatsidwa kwa makolo,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa