Yohane 4:43 - Buku Lopatulika43 Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Koma atapita masiku awiriwo anachoka komweko kunka ku Galileya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Atapita masiku aŵiriwo, Yesu adachoka napita ku Galileya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Patatha masiku awiri Iye anachoka napita ku Galileya. Onani mutuwo |