Yohane 4:34 - Buku Lopatulika34 Yesu ananena nao, Chakudya changa ndicho kuti ndichite chifuniro cha Iye amene anandituma Ine, ndi kutsiriza ntchito yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Yesu ananena nao, Chakudya changa ndicho kuti ndichite chifuniro cha Iye amene anandituma Ine, ndi kutsiriza ntchito yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Koma Yesu adati, “Chakudya changa nkuchita zimene afuna Atate amene adandituma, kuti nditsirize ntchito imene Iwo adandipatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Yesu anati, “Chakudya changa ndikuchita chifuniro cha Iye amene anandituma Ine ndi kumaliza ntchito yake. Onani mutuwo |