Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 4:33 - Buku Lopatulika

33 Chifukwa chake ophunzira ananena wina ndi mnzake, Kodi pali wina anamtengera Iye kanthu kakudya?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Chifukwa chake ophunzira ananena wina ndi mnzake, Kodi pali wina anamtengera Iye kanthu kakudya?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Pamenepo ophunzirawo adayamba kufunsana kuti, “Kodi kapena wina wadzaŵapatsa kale chakudya?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Ndipo ophunzira ake anafunsana wina ndi mnzake kuti, “Kodi alipo wina amene anamubweretsera Iye chakudya?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:33
6 Mawu Ofanana  

Ndipo kutacha, anaitana ophunzira ake; nasankha mwa iwo khumi ndi awiri, amene anawatchanso dzina lao atumwi:


Koma iwo sanadziwitse mau awa, ndipo anabisidwa kwa iwo, kuti asawadziwe; ndipo anaopa kumfunsa za mau awa.


Andrea mbale wake wa Simoni Petro anali mmodzi wa awiriwo, anamva Yohane, namtsata Iye.


Ndipo Yesu yemwe ndi ophunzira ake anaitanidwa kuukwatiwo.


Koma Iye anati kwa iwo, Ine ndili nacho chakudya chimene inu simuchidziwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa