Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:35 - Buku Lopatulika

35 Kodi simunena inu, kuti, Yatsala miyezi inai, ndipo kudza kumweta? Onani ndinena kwa inu, Kwezani maso anu, nimuyang'ane m'minda, kuti mwayera kale kufikira kumweta.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

35 Kodi simunena inu, kuti, Yatsala miyezi inai, ndipo kudza kumweta? Onani ndinena kwa inu, Kwezani maso anu, nimuyang'ane m'minda, kuti mwayera kale kufikira kumweta.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

35 Paja anthu amati, ‘Ikapita miyezi inai, ndiye kuti yafika nyengo yokolola.’ Koma ndithu, taonani m'mindamu, kodi simukuwona kuti mbeu zacha kale kudikira kholola?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

35 Kodi inu simunena kuti, ‘Kwatsala miyezi inayi ndipo kenaka kukolola?’ Ine ndikukuwuzani kuti, tsekulani maso anu ndipo muyangʼane mʼminda! Mbewu zacha kale kuti zikololedwe.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:35
4 Mawu Ofanana  

Tukula maso ako kuunguzaunguza, nuone; onsewa asonkhana pamodzi, nadza kwa iwe. Pali Ine, ati Yehova, iwe ndithu udzadziveka wekha ndi iwo onse, monga ndi chokometsera, ndi kudzimangira nao m'chuuno ngati mkwatibwi.


Anatuluka iwo m'mzinda ndipo analinkudza kwa Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa