Yohane 4:31 - Buku Lopatulika31 Pa mphindikati iyi ophunzira ake anampempha Iye, ndi kunena, Rabi, idyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Pa mphindikati iyi ophunzira ake anampempha Iye, ndi kunena, Rabi, idyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Nthaŵi imeneyo ophunzira ake a Yesu ankamupempha kuti, “Aphunzitsi, idyani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Pa nthawi imeneyi ndi kuti ophunzira ake akumukakamiza kuti, “Rabi idyani.” Onani mutuwo |