Yohane 4:20 - Buku Lopatulika20 Makolo athu analambira m'phiri ili; ndipo inu munena, kuti mu Yerusalemu muli malo oyenera kulambiramo anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Makolo athu analambira m'phiri ili; ndipo inu munena, kuti m'Yerusalemu muli malo oyenera kulambiramo anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Makolo athu ankapembedza Mulungu pa phiri ili, koma inu Ayuda mumati ndi ku Yerusalemu kumene anthu ayenera kumakapembedzerako.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Makolo athu ankapembedza mʼphiri ili koma inu Ayuda mumati malo amene tiyenera kupembedzera ali ku Yerusalemu.” Onani mutuwo |