Yohane 4:19 - Buku Lopatulika19 Mkazi ananena ndi Iye, Ambuye, ndizindikira kuti muli Mneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mkazi ananena ndi Iye, Ambuye, ndizindikira kuti muli Mneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Maiyo adati, “Bambo, ndadziŵa tsopano kuti ndinu mneneri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mayiyo anati, “Ambuye, ine ndazindikira kuti Inu ndinu mneneri. Onani mutuwo |