Yohane 4:18 - Buku Lopatulika18 pakuti wakhala nao amuna asanu; ndipo iye amene ukhala naye tsopano sali mwamuna wako; ichi wanena zoona. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 pakuti wakhala nao amuna asanu; ndipo iye amene ukhala naye tsopano sali mwamuna wako; ichi wanena zoona. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Paja mwakwatiwapo kale ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene muli naye tsopano si wanunso. Mwanenazi nzoona.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Zoona nʼzakuti iwe wakhala pa banja ndi amuna asanu, ndipo mwamuna amene uli naye tsopano si wako. Zimene wanenazi ndi zoona.” Onani mutuwo |