Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:17 - Buku Lopatulika

17 Mkazi anayankha nati kwa Iye, Ndilibe mwamuna. Yesu ananena naye, Wanena bwino, kuti mwamuna ndilibe;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Mkazi anayankha nati kwa Iye, Ndilibe mwamuna. Yesu ananena naye, Wanena bwino, kuti mwamuna ndilibe;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Maiyo adati, “Ndilibe mwamuna.” Yesu adati, “Mwanenetsa kuti mulibe mwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.” Yesu anati kwa iye, “Wakhoza ponena kuti ulibe mwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:17
4 Mawu Ofanana  

Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.


pakuti wakhala nao amuna asanu; ndipo iye amene ukhala naye tsopano sali mwamuna wako; ichi wanena zoona.


Tiyeni, mukaone munthu, amene anandiuza zinthu zilizonse ndinazichita: ameneyu sali Khristu nanga?


Chabwino; iwo anathyoledwa ndi kusakhulupirira kwao, ndipo iwe umaima ndi chikhulupiriro chako. Usamadzikuza mumtima, koma opatu:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa