Yohane 4:17 - Buku Lopatulika17 Mkazi anayankha nati kwa Iye, Ndilibe mwamuna. Yesu ananena naye, Wanena bwino, kuti mwamuna ndilibe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Mkazi anayankha nati kwa Iye, Ndilibe mwamuna. Yesu ananena naye, Wanena bwino, kuti mwamuna ndilibe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Maiyo adati, “Ndilibe mwamuna.” Yesu adati, “Mwanenetsa kuti mulibe mwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Iye anayankha kuti, “Ine ndilibe mwamuna.” Yesu anati kwa iye, “Wakhoza ponena kuti ulibe mwamuna. Onani mutuwo |