Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 4:16 - Buku Lopatulika

16 Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Yesu adati, “Pitani mukaitane amuna anu, nkukabweranso kuno.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 4:16
9 Mawu Ofanana  

Anadza naye kwa Yesu. M'mene anamyang'ana iye, anati, Uli Simoni mwana wa Yohane; udzatchedwa Kefa (ndiko kusandulika Petro).


Ananena naye kachitatu, Simoni mwana wa Yona, kodi undikonda Ine? Petro anamva chisoni kuti anati kwa iye kachitatu, Kodi undikonda Ine? Ndipo anati kwa iye, Ambuye, mudziwa Inu zonse; muzindikira kuti ndikukondani Inu. Yesu ananena naye, Dyetsa nkhosa zanga.


Mkaziyo ananena kwa Iye, Ambuye, ndipatseni madzi amene, kuti ndisamve ludzu, kapena ndisadze kuno kudzatunga.


Mkazi anayankha nati kwa Iye, Ndilibe mwamuna. Yesu ananena naye, Wanena bwino, kuti mwamuna ndilibe;


pakuti wakhala nao amuna asanu; ndipo iye amene ukhala naye tsopano sali mwamuna wako; ichi wanena zoona.


Ndipo palibe cholembedwa chosaonekera pamaso pake, koma zonse zikhala za pambalambanda ndi zovundukuka pamaso pake pa Iye amene tichita naye.


Ndipo ndidzaononga ana ake ndi imfa; ndipo idzazindikira Mipingo yonse kuti Ine ndine Iye amene ayesa impso ndi mitima; ndipo ndidzaninkha kwa yense wa inu monga mwa ntchito zanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa