Yohane 4:16 - Buku Lopatulika16 Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Yesu ananena kwa iye, Muka, kamuitane mwamuna wako, nudze kuno. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Yesu adati, “Pitani mukaitane amuna anu, nkukabweranso kuno.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Iye anamuwuza kuti, “Pita kayitane mwamuna wako ndipo ubwere naye.” Onani mutuwo |