Yohane 4:21 - Buku Lopatulika21 Yesu ananena naye, Tamvera Ine, mkazi iwe, kuti ikudza nthawi, imene simudzalambira Atate kapena m'phiri ili, kapena mu Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Yesu ananena naye, Tamvera Ine, mkazi iwe, kuti ikudza nthawi, imene simudzalambira Atate kapena m'phiri ili, kapena m'Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yesu adamuuza kuti, “Mai, ndithu ikudza nthaŵi pamene mudzapembedza Atate, osati pa phiri ili kapenanso ku Yerusalemu ai. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yesu anati, “Mayi inu khulupirira Ine. Nthawi ikubwera pamene inu simudzapembedza Atate mʼphiri ili kapena mu Yerusalemu. Onani mutuwo |