Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 3:9 - Buku Lopatulika

9 Nikodemo anayankha nati kwa Iye, Izi zingatheke bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Nikodemo anayankha nati kwa Iye, Izi zingatheke bwanji?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Nikodemo adafunsa kuti, “Zimenezi zingachitike bwanji?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Nekodimo anafunsa kuti, “Kodi izi zingatheke bwanji?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 3:9
9 Mawu Ofanana  

Koma mayendedwe a olungama akunga kuunika kwa mbandakucha, kunkabe kuwala kufikira usana woti mbee.


Ndipo ndidzayendetsa akhungu m'khwalala, limene iwo salidziwa, m'njira zimene iwo sazidziwa ndidzawatsogolera; ndidzawalitsa mdima m'tsogolo mwao, ndi kulungamitsa malo okhota. Zinthu izi Ine ndidzachita, ndipo sindidzawasiya.


Koma Maria anati kwa mngelo, Ichi chidzachitika bwanji, popeza ine sindidziwa mwamuna?


Yesu anayankha nati kwa iye, Kodi uli mphunzitsi wa Israele, ndipo sudziwa izi?


Nikodemo ananena kwa Iye, Munthu akhoza bwanji kubadwa atakalamba? Kodi akhoza kulowanso m'mimba ya amake ndi kubadwa?


Mphepo iomba pomwe ifuna, ndipo ukumva mau ake, koma sudziwa kumene ichokera, ndi kumene imuka; chotero aliyense wobadwa mwa Mzimu.


Pamenepo Ayuda anatetana wina ndi mnzake ndi kunena, Akhoza bwanji ameneyu kutipatsa ife kudya thupi lake?


Pamenepo ambiri a ophunzira ake, pakumva izi, anati, Mau awa ndi osautsa; akhoza kumva awa ndani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa