Yohane 3:9 - Buku Lopatulika9 Nikodemo anayankha nati kwa Iye, Izi zingatheke bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nikodemo anayankha nati kwa Iye, Izi zingatheke bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nikodemo adafunsa kuti, “Zimenezi zingachitike bwanji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nekodimo anafunsa kuti, “Kodi izi zingatheke bwanji?” Onani mutuwo |