Yohane 3:27 - Buku Lopatulika27 Yohane anayankha nati, Munthu sangathe kulandira kanthu, ngati sikapatsidwa kwa iye kuchokera Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Yohane anayankha nati, Munthu sakhoza kulandira kanthu, ngati sikapatsidwa kwa iye kuchokera Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Yohane adati, “Munthu sangalandire kanthu kalikonse ngati Mulungu sampatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atamva zimenezi, Yohane anayankha kuti, “Munthu amalandira chokhacho chapatsidwa kwa iye kuchokera kumwamba. Onani mutuwo |