Yohane 21:25 - Buku Lopatulika25 Koma palinso zina zambiri zimene Yesu anazichita, zoti zikadalembedwa zonse phee, ndilingalira kuti dziko lapansi silikadakhala nao malo a mabuku amene akadalembedwa. Amen. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Koma palinso zina zambiri zimene Yesu anazichita, zoti zikadalembedwa zonse phee, ndilingalira kuti dziko lapansi silikadakhala nao malo a mabuku amene akadalembedwa. Amen. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma palinso zina zambiri zimene Yesu ankachita. Zikadalembedwa zonsezo, ndiganiza kuti pa dziko lonse lapansi sipakadaoneka malo okwanira mabuku onse olembedwawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Koma palinso zina zambiri zimene Yesu anachita. Zikanalembedwa zonsezi, ndikhulupirira dziko lonse lapansi likanasowa malo osungirako mabuku onse amene akanalembedwa. Onani mutuwo |