Machitidwe a Atumwi 1:1 - Buku Lopatulika1 Taonani Teofilo inu, mau aja oyamba ndinakonza, za zonse Yesu anayamba kuzichita ndi kuziphunzitsa, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Taonani Teofilo inu, mau aja oyamba ndinakonza, za zonse Yesu anayamba kuzichita ndi kuziphunzitsa, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 A Teofilo, M'buku langa loyamba lija ndidakulemberani za zonse zimene Yesu ankachita ndi kuphunzitsa kuyambira pa chiyambi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼbuku langa loyamba, ndinakulembera iwe Teofilo zonse zimene Yesu anayamba kuchita ndi kuphunzitsa, Onani mutuwo |