Machitidwe a Atumwi 1:2 - Buku Lopatulika2 kufikira tsiku lija anatengedwa kunka Kumwamba, atatha kulamula mwa Mzimu Woyera atumwi amene adawasankha; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kufikira tsiku lija anatengedwa kunka Kumwamba, atatha kulamula mwa Mzimu Woyera atumwi amene adawasankha; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 kufikira tsiku limene adatengedwa kupita Kumwamba. Mwa mphamvu ya Mzimu Woyera, anali atauza atumwi amene adaŵasankha aja zoti iwowo adzachite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 mpaka tsiku limene anatengedwa kupita kumwamba, mwamphamvu ya Mzimu Woyera, atawalangiza atumwi amene anawasankha. Onani mutuwo |