Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yohane 21:24 - Buku Lopatulika

24 Yemweyu ndiye wophunzira wakuchita umboni za izi, ndipo analembera izi; ndipo tidziwa kuti umboni wake ndi woona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Yemweyu ndiye wophunzira wakuchita umboni za izi, ndipo analembera izi; ndipo tidziwa kuti umboni wake ndi woona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Ameneyo ndiye wophunzira uja amene akuchitira umboni zimene zidachitikazo, ndipo ndiye amene adazilemba. Tikudziŵa kuti umboni wakewo ngwoona.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Uyu ndi wophunzira amene akuchitira umboni ndipo ndi amene analemba. Ife tidziwa kuti umboni wake ndi woona.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 21:24
5 Mawu Ofanana  

Ndipo inunso muchita umboni, pakuti muli ndi Ine kuyambira chiyambi.


Ndipo iye amene anaona, wachita umboni, ndi umboni wake uli woona; ndipo iyeyu adziwa kuti anena zoona, kuti inunso mukakhulupirire.


Iye ndiye amene adadza mwa madzi ndi mwazi, ndiye Yesu Khristu; wosati ndi madzi okha, koma ndi madzi ndi mwazi. Ndipo Mzimu ndiye wakuchita umboni, chifukwa Mzimu ndiye choonadi.


Demetrio, adamchitira umboni anthu onse, ndi choonadi chomwe; ndipo ifenso tichita umboni; ndipo udziwa kuti umboni wathu uli woona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa