Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 21:21 - Buku Lopatulika

21 Pamenepo Petro pakumuona, ananena kwa Yesu, Ambuye, koma nanga uyu?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Pamenepo Petro pakumuona, ananena kwa Yesu, Ambuye, koma nanga uyu?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pamene Petro adamuwona iyeyo, adafunsa Yesu kuti, “Ambuye, nanga uyu bwanji?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Petro atamuona iye, anafunsa kuti, “Ambuye, nanga uyu?”

Onani mutuwo Koperani




Yohane 21:21
5 Mawu Ofanana  

Petro, m'mene anacheuka, anapenya wophunzira amene Yesu anamkonda alikutsata, amenenso anatsamira pachifuwa pake pamgonero, nati, Ambuye, ndani iye wakupereka Inu?


Yesu ananena naye, Ngati ndifuna uyu akhale kufikira ndidza Ine, kuli chiyani ndi iwe? Unditsate Ine iwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa