Yohane 21:22 - Buku Lopatulika22 Yesu ananena naye, Ngati ndifuna uyu akhale kufikira ndidza Ine, kuli chiyani ndi iwe? Unditsate Ine iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Yesu ananena naye, Ngati ndifuna uyu akhale kufikira ndidza Ine, kuli chiyani ndi iwe? Unditsate Ine iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Yesu adamuuza kuti, “Ngati ndifuna kuti iye akhalebe mpaka ndidzabwerenso, kodi iwe uli nazo kanthu? Iweyo unditsate.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Yesu anayankha kuti, “Ine nditafuna kuti akhalebe ndi moyo mpaka nditabweranso, zikukukhudza bwanji zimenezo? Iwe uyenera kunditsata Ine.” Onani mutuwo |