Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yohane 21:13 - Buku Lopatulika

13 Yesu anadza natenga mkate napatsa iwo, momwemonso nsomba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Yesu anadza natenga mkate napatsa iwo, momwemonso nsomba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Yesu adadza natenga buledi uja nkuŵapatsa. Adateronso ndi nsomba zija.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Yesu anabwera, natenga buledi ndikuwapatsa iwo, ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsomba.

Onani mutuwo Koperani




Yohane 21:13
6 Mawu Ofanana  

Yesu ananena nao, Tenganiko nsomba zimene mwazigwira tsopano.


Ndipo pamene anatulukira pamtunda, anapenya moto wamakala pomwepo, ndi kansomba kosanjikikako, ndi mkate.


Pomwepo Yesu anatenga mikateyo; ndipo pamene adayamika, anagawira iwo akukhala pansi; momwemonso ndi tinsomba, monga momwe iwo anafuna.


Pali mnyamata pano, amene ali nayo mikate isanu yabarele, ndi tinsomba tiwiri; koma nanga izi zikwanira bwanji ambiri otere?


si kwa anthu onse ai, koma kwa mboni zosankhidwiratu ndi Mulungu, ndiwo ife amene tinadya ndi kumwa naye pamodzi, atauka iye kwa akufa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa